Masalimo 26:11 - Buku Lopatulika11 Koma ine, ndidzayenda mu ungwiro wanga; mundiombole, ndipo ndichitireni chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma ine, ndidzayenda m'ungwiro wanga; mundiombole, ndipo ndichitireni chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma ine ndimayenda mokhulupirika, mundikomere mtima ndipo mundipulumutse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa; mu msonkhano wa anthu anu ndidzatamanda Yehova. Onani mutuwo |