Masalimo 24:8 - Buku Lopatulika8 Mfumu imene ya ulemerero ndani? Yehova wamphamvu ndi wolimba, Yehova wolimba kunkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mfumu imene ya ulemerero ndani? Yehova wamphamvu ndi wolimba, Yehova wolimba kunkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani? Ndi Chauta wanyonga ndi wamphamvu, Chauta ndiye ngwazi pa nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani? Yehova Wamphamvuzonse, Yehova ndiye wamphamvu pa nkhondo. Onani mutuwo |