Masalimo 24:7 - Buku Lopatulika7 Weramutsani mitu yanu, zipata inu; ndipo kwezekani inu, zitseko zosatha, kuti Mfumu ya ulemerero ilowe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Weramutsani mitu yanu, zipata inu; ndipo kwezekani inu, zitseko zosatha, kuti Mfumu ya ulemerero ilowe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Kankhani zipata za mzinda, tsekulani zitseko zakalekalezo, kuti Mfumu yaulemerero iloŵe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tukulani mitu yanu inu zipata; tsekukani, inu zitseko zakalekalenu, kuti Mfumu yaulemerero ilowe. Onani mutuwo |