Masalimo 24:5 - Buku Lopatulika5 Iye adzalandira dalitso kwa Yehova, ndi chilungamo kwa Mulungu wa chipulumutso chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Iye adzalandira dalitso kwa Yehova, ndi chilungamo kwa Mulungu wa chipulumutso chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adzalandira madalitso kwa Chauta, ndipo Mulungu Mpulumutsi wake adzagamula kuti alibe mlandu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova ndipo Mulungu mpulumutsi wake adzagamula kuti alibe mlandu. Onani mutuwo |