Masalimo 21:9 - Buku Lopatulika9 Mudzawaika ngati ng'anjo yamoto pa nyengo ya mkwiyo wanu. Yehova adzawatha m'kukwiya kwake, ndipo moto udzawanyeketsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mudzawaika ngati ng'anjo yamoto pa nyengo ya mkwiyo wanu. Yehova adzawatha m'kukwiya kwake, ndipo moto udzawanyeketsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ikangotulukira, idzaŵaononga monga m'mene ng'anjo yamoto imaonongera. Chauta adzaŵatha phu, chifukwa cha kukwiya nawo, ndipo iwo adzanyeka ndi moto kuchita kuti psiti. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pa nthawi ya kuonekera kwanu mudzawasandutsa ngʼanjo yamoto yotentha. Mu ukali wake Yehova adzawameza, ndipo moto wake udzawatha. Onani mutuwo |