Masalimo 21:10 - Buku Lopatulika10 Mudzaziononga zobala zao kuzichotsa padziko lapansi, ndi mbeu zao mwa ana a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mudzaziononga zobala zao kuzichotsa pa dziko lapansi, ndi mbeu zao mwa ana a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mfumuyo idzaononga ana ao pa dziko lapansi, zidzukulu zao zidzatha pakati pa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Inu mudzawononga ana awo pa dziko lapansi, zidzukulu zawo pakati pa anthu. Onani mutuwo |