Masalimo 21:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti mfumu akhulupirira Yehova, ndipo mwa chifundo cha Wam'mwambamwamba sadzagwedezeka iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti mfumu akhulupirira Yehova, ndipo mwa chifundo cha Wam'mwambamwamba sadzagwedezeka iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Paja mfumuyo imakhulupirira Chauta, ndipo siidzagwedezeka chifukwa cha chikondi chosasinthika cha Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pakuti mfumu imadalira Yehova; kudzera mʼchikondi chake chosatha cha Wammwambamwamba, iyo sidzagwedezeka. Onani mutuwo |