Masalimo 21:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti mufika kwa iye ndi madalitso okoma; muika korona wa golide woyengetsa pamutu pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti mufika kwa iye ndi madalitso okoma; muika korona wa golide woyengetsa pamutu pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mumafika kwa mfumuyo ndi madalitso okoma kwambiri. Mwaiveka chipewa chaufumu chagolide pamutu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inu munayilandira ndi madalitso ochuluka ndipo munayiveka chipewa chaufumu chagolide weniweni pa mutu wake. Onani mutuwo |