Masalimo 21:4 - Buku Lopatulika4 Anakupemphani moyo, mwampatsa iye; mwamtalikitsira masiku kunthawi za nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Anakupemphani moyo, mwampatsa iye; mwamtalikitsira masiku kunthawi za nthawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iyo idakupemphani moyo, ndipo Inu mudaipatsa moyo wautali, wamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye anakupemphani moyo, ndipo munamupatsa masiku ochuluka kwamuyaya. Onani mutuwo |