Masalimo 21:1 - Buku Lopatulika1 Yehova, adzasekera mfumu mu mphamvu yanu; adzakondwera kwakukulu m'chipulumutso chanu! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova, adzasekera mfumu mu mphamvu yanu; adzakondwera kwakukulu m'chipulumutso chanu! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mfumu ikusangalala chifukwa mwaipatsa mphamvu, Inu Chauta, ikukondwa kwambiri chifukwa mwaipambanitsa ndinu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova, mfumu ikusangalala mu mphamvu yanu, chimwemwe chake nʼchachikuludi pa kupambana kumene mumapereka! Onani mutuwo |