Masalimo 16:8 - Buku Lopatulika8 Ndaika Yehova patsogolo panga nthawi zonse; popeza ali padzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndaika Yehova patsogolo panga nthawi zonse; popeza ali pa dzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nthaŵi zonse ndimalingalira za Chauta. Popeza kuti ali ku dzanja langa lamanja, palibe amene angandiopse konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka. Onani mutuwo |