Masalimo 16:7 - Buku Lopatulika7 Ndidzadalitsa Yehova, amene anandichitira uphungu, usikunso impso zanga zindilangiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndidzadalitsa Yehova, amene anandichitira uphungu, usikunso impso zanga zindilangiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndikutamanda Chauta amene ali phungu wanga. Mtima wanga umandilangiza ndi usiku womwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza. Onani mutuwo |