Masalimo 16:2 - Buku Lopatulika2 Ndinati kwa Yehova, Inu ndinu Ambuye wanga, ndilibe chabwino china choposa Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndinati kwa Yehova, Inu ndinu Ambuye wanga, ndilibe chabwino china choposa Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndimamuuza Chauta kuti, “Inu ndinu Ambuye anga. Ndilibe chinthu china chabwino koma Inu nokha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.” Onani mutuwo |