Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 16:1 - Buku Lopatulika

1 Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mundisunge Inu Mulungu, pakuti ndikuthaŵira kwa Inu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 16:1
21 Mawu Ofanana  

Yehova asunga opusa; ndidafooka ine, koma anandipulumutsa.


Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha.


Wodala munthu amene akhala naye Mulungu wa Yakobo kuti amthandize, chiyembekezo chake chili pa Yehova, Mulungu wake.


M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Ndisungeni monga kamwana ka m'diso, ndifungatireni mu mthunzi wa mapiko anu,


Adadzitengera kwa Yehova; kuti adzampulumutsa, amlanditse tsopano popeza akondwera naye.


Sungani moyo wanga, ndilanditseni, ndisakhale nao manyazi, pakuti ndakhulupirira Inu.


Kondani Yehova, Inu nonse okondedwa ake, Yehova asunga okhulupirika, ndipo abwezera zochuluka iye wakuchita zodzitama.


Pakuti Yehova akonda chiweruzo, ndipo sataya okondedwa ake. Asungika kosatha, koma adzadula mbumba za oipa.


Mundichitire chifundo, Mulungu, pakuti anthu afuna kundimeza. Andipsinja pondithira nkhondo tsiku lonse.


Mwatitaya Mulungu, mwatipasula; mwakwiya; tibwezereni.


Yehova Mulungu wanga, ndakhulupirira Inu; mundipulumutse kwa onse akundilonda, nimundilanditse;


kuti angamwetule moyo wanga ngati mkango, ndi kuukadzula, wopanda wina wondilanditsa.


Yehova wa makamu, wodala munthu wakukhulupirira Inu.


ndipo iwo akudziwa dzina lanu adzakhulupirira Inu; pakuti, Inu Yehova, simunawasiye iwo akufuna Inu.


Inu okonda Yehova, danani nacho choipa: Iye asunga moyo wa okondedwa ake; awalanditsa m'manja mwa oipa.


kuti atchinjirize njira za chiweruzo, nadikire khwalala la opatulidwa ake.


koma tokha tinakhala nacho chitsutso cha imfa mwa ife tokha, kuti tisalimbike pa ife tokha, koma pa Mulungu wakuukitsa akufa;


Chifukwa cha ichicho ndinamva zowawa izi; komatu sindichita manyazi; pakuti ndimdziwa Iye amene ndamkhulupirira, ndipo ndikopeka mtima kuti ali wa mphamvu ya kudikira chosungitsa changacho kufikira tsiku lijalo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa