Masalimo 16:1 - Buku Lopatulika1 Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mundisunge Inu Mulungu, pakuti ndikuthaŵira kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu. Onani mutuwo |