Masalimo 150:3 - Buku Lopatulika3 Mlemekezeni ndi kulira kwa lipenga; mlemekezeni ndi chisakasa ndi zeze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mlemekezeni ndi kulira kwa lipenga; mlemekezeni ndi chisakasa ndi zeze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mtamandeni pomuimbira lipenga, mtamandeni ndi gitara ndi zeze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze. Onani mutuwo |
Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;