Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 150:4 - Buku Lopatulika

4 Mlemekezeni ndi lingaka ndi kuthira mang'ombe: Mlemekezeni ndi zoimbira za zingwe ndi chitoliro.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Mlemekezeni ndi lingaka ndi kuthira mang'ombe: Mlemekezeni ndi zoimbira za zingwe ndi chitoliro.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mtamandeni poimba ng'oma ndi povina, mtamandeni ndi zipangizo zansambo ndi mngoli.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 150:4
10 Mawu Ofanana  

Aimbira lingaka ndi zeze, nakondwera pomveka chitoliro.


Chifukwa chake zeze wanga wasandulika wa maliro, ndi chitoliro changa cha mau a olira misozi.


Ndidzakuimbirani nyimbo yatsopano, Mulungu; pa chisakasa cha zingwe khumi ndidzaimbira zakukulemekezani.


Alemekeze dzina lake ndi kuthira mang'ombe; amuimbire zomlemekeza ndi lingaka ndi zeze.


Yamikani Yehova ndi zeze; muimbireni ndi chisakasa cha zingwe khumi.


Zovala zanu zonse nza mure, ndi khonje, ndi kasiya; m'zinyumba za mfumu zomanga ndi minyanga ya njovu mwatuluka zoimba za zingwe zokukondweretsani.


Pa choimbira cha zingwe khumi ndi pachisakasa; pazeze ndi kulira kwake.


Ndipo Miriyamu mneneriyo, mlongo wa Aroni, anagwira lingaka m'dzanja lake; ndipo akazi onse anatuluka kumtsata ndi malingaka ndi kuthira mang'ombe.


Yehova ndiye wondipulumutsa ine; Chifukwa chake tidzaimba nyimbo zanga, ndi zoimba zazingwe Masiku onse a moyo wathu m'nyumba ya Yehova.


Yehova, Ambuye, ndiye mphamvu yanga, asanduliza mapazi anga ngati a mbawala, nadzandipondetsa pa misanje yanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa