Masalimo 150:2 - Buku Lopatulika2 Mlemekezeni chifukwa cha ntchito zake zolimba; mlemekezeni monga mwa ukulu wake waunjinji. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mlemekezeni chifukwa cha ntchito zake zolimba; mlemekezeni monga mwa ukulu wake waunjinji. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mtamandeni chifukwa cha ntchito zake zamphamvu, mtamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana. Onani mutuwo |