Masalimo 149:2 - Buku Lopatulika2 Akondwere Israele mwa Iye amene anamlenga; ana a Ziyoni asekere mwa mfumu yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Akondwere Israele mwa Iye amene anamlenga; ana a Ziyoni asekere mwa mfumu yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Aisraele asangalale ndi Mlengi wao. Anthu a Ziyoni akondwere ndi Mfumu yao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Israeli asangalale mwa mlengi wake; anthu a ku Ziyoni akondwere mwa Mfumu yawo. Onani mutuwo |