Masalimo 149:1 - Buku Lopatulika1 Aleluya, Muimbireni Yehova nyimbo yatsopano, ndi chilemekezo chake mu msonkhano wa okondedwa ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Aleluya, Muimbireni Yehova nyimbo yatsopano, ndi chilemekezo chake mu msonkhano wa okondedwa ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tamandani Chauta! Imbirani Chauta nyimbo yatsopano, imbani nyimbo yomtamanda pa msonkhano wa anthu ake oyera mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tamandani Yehova. Imbirani Yehova nyimbo yatsopano, matamando ake mu msonkhano wa oyera mtima. Onani mutuwo |