Masalimo 147:9 - Buku Lopatulika9 Amene apatsa zoweta chakudya chao, ana a khwangwala alikulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Amene apatsa zoweta chakudya chao, ana a khungubwi alikulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amapereka chakudya kwa nyama ndi kwa ana a khungubwi pamene akulira chakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye amapereka chakudya kwa ngʼombe ndi kwa ana a makwangwala pamene akulira chakudya. Onani mutuwo |