Masalimo 143:11 - Buku Lopatulika11 Mundipatse moyo, Yehova, chifukwa cha dzina lanu; mwa chilungamo chanu mutulutse moyo wanga m'sautso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mundipatse moyo, Yehova, chifukwa cha dzina lanu; mwa chilungamo chanu mutulutse moyo wanga m'sautso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Sungani moyo wanga, Inu Chauta, kuti dzina lanu lilemekezeke. Munditulutse pa mavuto chifukwa cha kulungama kwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu; mwa chilungamo chanu tulutseni mʼmasautso anga. Onani mutuwo |