Masalimo 143:1 - Buku Lopatulika1 Imvani pemphero langa, Yehova; nditcherere khutu kupemba kwanga; ndiyankheni mwa chikhulupiriko chanu, mwa chilungamo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Imvani pemphero langa, Yehova; nditcherere khutu kupemba kwanga; ndiyankheni mwa chikhulupiriko chanu, mwa chilungamo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Imvani pemphero langa, Inu Chauta. Tcherani khutu kuti mumve kupemba kwanga. Mundiyankhe chifukwa cha kukhulupirika kwanu ndi kulungama kwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova imvani pemphero langa, mvetserani kulira kwanga kopempha chifundo; mwa kukhulupirika kwanu ndi chilungamo chanu bwerani kudzandithandiza. Onani mutuwo |