Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 142:7 - Buku Lopatulika

7 Tulutsani moyo wanga m'ndende, kuti ndiyamike dzina lanu; olungama adzandizinga; pakuti mudzandichitira zokoma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Tulutsani moyo wanga m'ndende, kuti ndiyamike dzina lanu; olungama adzandizinga; pakuti mudzandichitira zokoma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Tulutseni m'ndende kuti ndizitamanda dzina lanu. Anthu anu adzandizungulira, chifukwa Inu mwandichitira zabwino zambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Tulutseni mʼndende yanga kuti nditamande dzina lanu. Ndipo anthu olungama adzandizungulira chifukwa cha zabwino zanu pa ine.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 142:7
20 Mawu Ofanana  

Ubwere moyo wanga ku mpumulo wako; pakuti Yehova anakuchitira chokoma.


Muchitire chokoma mtumiki wanu kuti ndikhale ndi moyo; ndipo ndidzasamalira mau anu.


Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; popeza ndayembekezera mau anu.


Ndidzaimbira Yehova, pakuti anandichitira zokoma.


Ndifuula nalo liu langa kwa Yehova; ndi mau anga ndipemba kwa Yehova.


Mundipatse moyo, Yehova, chifukwa cha dzina lanu; mwa chilungamo chanu mutulutse moyo wanga m'sautso.


Mundilanditse kwa adani anga, Yehova; ndibisala mwa Inu.


ndiye wakuchitira chiweruzo osautsika; ndiye wakupatsa anjala chakudya; Yehova amasula akaidi.


Ndipo simunandipereke m'dzanja la mdani; munapondetsa mapazi anga pali malo.


Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.


Ndipo iwo akubwezera choipa pa chabwino atsutsana nane, popeza nditsata chabwino.


Kuti ndibukitse lemekezo lanu lonse; pa bwalo la mwana wamkazi wa Ziyoni, ndidzakondwera nacho chipulumutso chanu.


Pobwerera m'mbuyo adani anga, akhumudwa naonongeka pankhope panu.


Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine; pakuti Yehova wandidzoza ine ndilalikire mau abwino kwa ofatsa; Iye wanditumiza ndikamange osweka mtima, ndikalalikire kwa am'nsinga mamasulidwe, ndi kwa omangidwa kutsegulidwa kwa m'ndende;


yemweyo Mulungu anamuukitsa, atamasula zowawa za imfa, mwakuti sikunali kotheka kuti Iye agwidwe nayo.


Taonani tiwayesera odala opirirawo; mudamva za chipiriro cha Yobu, ndipo mwaona chitsiriziro cha Ambuye, kuti Ambuye ali wodzala chikondi, ndi wachifundo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa