Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 141:7 - Buku Lopatulika

7 Mafupa athu amwazika pakamwa pa manda, monga ngati akumba nanyimphula nthaka yapansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Mafupa athu amwazika pakamwa pa manda, monga ngati akumba nanyimphula nthaka yapansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziŵaza, ndi m'menenso mafupa ao adzamwazikira ku manda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 141:7
7 Mawu Ofanana  

Koma, chifukwa cha Inu, tiphedwa tsiku lonse; tiyesedwa ngati nkhosa zakuzipha.


Pamenepo anaopa kwakukulu, popanda chifukwa cha kuopa, pakuti Mulungu anamwaza mafupa a iwo akuzinga iwe; unawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawakaniza.


Monganso kwalembedwa, Chifukwa cha Inu tilikuphedwa dzuwa lonse; tinayesedwa monga nkhosa zakupha.


koma tokha tinakhala nacho chitsutso cha imfa mwa ife tokha, kuti tisalimbike pa ife tokha, koma pa Mulungu wakuukitsa akufa;


anaponyedwa miyala, anachekedwa pakati, anayesedwa, anaphedwa ndi lupanga, anayendayenda ovala zikopa zankhosa, ndi zikopa zambuzi, nakhala osowa, osautsidwa, ochitidwa zoipa,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa