Masalimo 141:2 - Buku Lopatulika2 Pemphero langa liikike ngati chofukiza pamaso panu; kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pemphero langa liikike ngati chofukiza pamaso panu; kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pemphero langa likwere kwa Inu ngati lubani, kukweza kwa manja anga kukhale ngati nsembe yamadzulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani; kukweza manja kwanga kukhale ngati nsembe yamadzulo. Onani mutuwo |