Masalimo 141:1 - Buku Lopatulika1 Yehova, ndaitana kwa Inu; ndifulumireni ine; munditcherere khutu, pamene ndiitana kwa Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova, ndaitana kwa Inu; ndifulumireni ine; munditcherere khutu, pamene ndiitana kwa Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndikukuitanani, Inu Chauta, fulumirani kudzandithandiza. Tcherani khutu kuti mumve liwu langa pamene ndikupemphera kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine. Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu. Onani mutuwo |