Masalimo 140:12 - Buku Lopatulika12 Ndidziwa kuti Yehova adzanenera wozunzika mlandu, ndi kuweruzira aumphawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndidziwa kuti Yehova adzanenera wozunzika mlandu, ndi kuweruzira aumphawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndimadziŵa kuti Inu Chauta mumateteza ozunzika, mumaweruza mwachilungamo anthu osoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndikudziwa kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama kwa anthu osauka, ndipo amateteza zolinga za anthu osowa. Onani mutuwo |