Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 140:11 - Buku Lopatulika

11 Munthu wamlomo sadzakhazikika padziko lapansi; choipa chidzamsaka munthu wachiwawa kuti chimgwetse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Munthu wamlomo sadzakhazikika pa dziko lapansi; choipa chidzamsaka munthu wachiwawa kuti chimgwetse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Musalole kuti woononga mbiri ya mnzake akhazikike m'dziko. Choipa chimlondole munthu wankhanza mpaka kumuwononga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Musalole kuti anthu achipongwe akhazikike mʼdziko; choyipa chilondole anthu ankhanza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 140:11
10 Mawu Ofanana  

Mphulupulu idzamupha woipa; ndipo adzawatsutsa kumlandu iwo akudana naye wolungama.


Anadziwika Yehova, anachita kuweruza, woipayo anakodwa ndi ntchito ya manja ake.


M'kulakwa kwa milomo muli msampha woipa; koma wolungama amatuluka m'mavuto.


Zoipa zilondola ochimwa; koma olungama adzalandira mphotho yabwino.


Wokhota mtima sadzapeza bwino; ndipo mwini lilime lokhota adzagwa m'zoipa.


Lilime lili ndi mphamvu pa imfa ndi moyo; wolikonda adzadya zipatso zake.


Maso akunyada, lilime lonama, ndi manja akupha anthu osachimwa;


Tsoka kwa woipa! Kudzamuipira; chifukwa kuti mphotho ya manja ake idzapatsidwa kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa