Masalimo 14:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepa anaopaopatu, pakuti Mulungu ali mu mbadwo wa wolungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepa anaopaopatu, pakuti Mulungu ali mu mbadwo wa wolungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsonotu iwo adzachita mantha aakulu, pakuti Mulungu amakhala pa mbali ya anthu abwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Awo ali apowo, agwidwa ndi mantha aakulu, pakuti Mulungu ali mʼgulu la olungama. Onani mutuwo |