Masalimo 14:2 - Buku Lopatulika2 Yehova mu Mwamba anaweramira pa ana a anthu, kuti aone ngati aliko wanzeru, wakufuna Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yehova m'Mwamba anaweramira pa ana a anthu, kuti aone ngati aliko wanzeru, wakufuna Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta kumwambako waŵerama, akuyang'ana anthu pansi pano, kuti aone ngati angakhalepo mmodzi wanzeru wofunitsitsa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova kumwamba wayangʼana pansi, kuyangʼana anthu onse kuti aone ngati alipo wina wanzeru, amene amafunafuna Mulungu. Onani mutuwo |