Masalimo 14:3 - Buku Lopatulika3 Anapatuka onse; pamodzi anavunda mtima; palibe wakuchita bwino ndi mmodzi yense. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anapatuka onse; pamodzi anavunda mtima; palibe wakuchita bwino ndi mmodzi yense. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma ai, anthu onse ndi osokera, onsewo ndi oipa chimodzimodzi. Palibe ndi mmodzi yemwe wochita zabwino, ai, palibiretu ndi mmodzi yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Onse atembenukira kumbali, onse pamodzi asanduka oyipa; palibe amene amachita zabwino, palibiretu ndi mmodzi yemwe. Onani mutuwo |