Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 137:8 - Buku Lopatulika

8 Mwana wamkazi wa ku Babiloni, iwe amene udzapasulidwa; wodala iye amene adzakubwezera chilango monga umo unatichitira ife.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mwana wamkazi wa ku Babiloni, iwe amene udzapasulidwa; wodala iye amene adzakubwezera chilango monga umo unatichitira ife.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mzinda wa Babiloni, iwe woyenera kuwonongedwawe, adzakhala wodala munthu amene adzakubwezera zimene watichita ifezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iwe mwana wa mkazi wa Babuloni, woyenera kuwonongedwa, wodalitsika ndi yemwe adzakubwezera pa zimene watichitira.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 137:8
14 Mawu Ofanana  

Katundu wa chipululu cha kunyanja. Monga akamvulumvulu a kumwera apitirira, kufumira kuchipululu kudziko loopsa.


ndi kunena za Kirusi, Iye ndiye mbusa wanga, ndipo adzachita zofuna zanga zonse; ndi kunena za Yerusalemu, Adzamangidwa; ndi kwa Kachisi, Maziko ako adzaikidwa.


Mau amene ananena Yehova za Babiloni, za dziko la Ababiloni, mwa Yeremiya mneneri.


Memezani amauta amenyane ndi Babiloni, onse amene akoka uta; mummangire iye zithando pomzungulira iye, asapulumuke mmodzi wake yense; mumbwezere iye monga mwa ntchito yake; monga mwa zonse wazichita, mumchitire iye; pakuti anamnyadira Yehova, Woyera wa Israele.


Haya Ziyoni, thawa iwe wakukhala ndi mwana wamkazi wa Babiloni.


Kondwera pa iye, m'mwamba iwe, ndi oyera mtima, ndi atumwi, ndi aneneri inu; chifukwa Mulungu anauweruzira kuweruzidwa kwanu.


Muubwezere, monganso uwu unabwezera, ndipo muwirikize kawiri, monga mwa ntchito zake; m'chikhomo unathiramo, muuthirire chowirikiza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa