Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 137:4 - Buku Lopatulika

4 Tidati, Tidzaimba bwanji nyimbo ya Yehova m'dziko lachilendo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Tidati, Tidzaimba bwanji nyimbo ya Yehova m'dziko lachilendo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono ife tidati, “Tingaimbe bwanji nyimbo ya Chauta kuchilendo ngati kuno?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova mʼdziko lachilendo?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 137:4
6 Mawu Ofanana  

mphindi yakugwa misozi ndi mphindi yakuseka; mphindi yakulira ndi mphindi yakuvina;


Ndipo tsiku limenelo Ambuye, Yehova wa makamu, anaitana kulira, ndi kugwa misozi, ndi kumeta, ndi kuvala chiguduli m'chuuno;


Pamenepo udzati m'mtima mwako, Ndani wandibalitsa ine amenewa, popeza ana anga anachotsedwa kwa ine, ndipo ndili wouma, ndi wochotsedwa m'dziko, ndi woyendayenda kwina ndi kwina? Ndipo ndani wadza ndi awa? Taona ndinasiyidwa ndekha, amenewa anali kuti?


Sadzatsanulira Yehova nsembe zavinyo; sizidzamkomera Iye nsembe zao; zidzakhala kwa iwo ngati mkate wa achisoni; onse akudyako adzadetsedwa; pakuti mkate wao udzakhala wa njala yao, uwu sudzalowa m'nyumba ya Yehova.


Koma nyimbo za ku Kachisi zidzasanduka kubuma tsiku ilo, ati Ambuye Yehova; mitembo idzachuluka; adzaitaya paliponse padzakhala zii.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa