Masalimo 137:4 - Buku Lopatulika4 Tidati, Tidzaimba bwanji nyimbo ya Yehova m'dziko lachilendo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tidati, Tidzaimba bwanji nyimbo ya Yehova m'dziko lachilendo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono ife tidati, “Tingaimbe bwanji nyimbo ya Chauta kuchilendo ngati kuno?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova mʼdziko lachilendo? Onani mutuwo |