Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 137:5 - Buku Lopatulika

5 Ndikakuiwalani, Yerusalemu, dzanja lamanja langa liiwale luso lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndikakuiwalani, Yerusalemu, dzanja lamanja langa liiwale luso lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndikakuiŵala iwe Yerusalemu, dzanja langa lamanja liwume.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu, dzanja langa lamanja liyiwale luso lake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 137:5
11 Mawu Ofanana  

Pakuti tsiku limodzi m'mabwalo anu likoma koposa masiku ambirimbiri akukhala pena. Kukhala ine wapakhomo m'nyumba ya Mulungu wanga, kundikonda ine koposa kugonera m'mahema a choipa.


Chifukwa cha Ziyoni sindidzakhala chete, ndi chifukwa cha Yerusalemu sindidzapuma, kufikira chilungamo chake chidzatuluka monga kuyera, ndi chipulumutso chake monga nyali yoyaka.


Inu amene mwapulumuka kulupanga, pitani inu musaime chiimire; mukumbukire Yehova kutali, Yerusalemu alowe m'mtima mwanu.


Tsoka mbusa wopanda pake, wakusiya zoweta! Lupanga padzanja lake, ndi pa diso lake la kumanja; dzanja lake lidzauma konse, ndi diso lake lamanja lidzada bii.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa