Masalimo 137:5 - Buku Lopatulika5 Ndikakuiwalani, Yerusalemu, dzanja lamanja langa liiwale luso lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndikakuiwalani, Yerusalemu, dzanja lamanja langa liiwale luso lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndikakuiŵala iwe Yerusalemu, dzanja langa lamanja liwume. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu, dzanja langa lamanja liyiwale luso lake. Onani mutuwo |