Masalimo 137:3 - Buku Lopatulika3 Popeza pamenepo akutigwirawo anatifunsa nyimbo ndipo akutizunza anafuna tisekere, ndi kuti, Mutiimbire nyimbo imodzi ya ku Ziyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Popeza pamenepo akutigwirawo anatifunsa nyimbo ndipo akutizunza anafuna tisekere, ndi kuti, Mutiimbire nyimbo imodzi ya ku Ziyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kumeneko anthu otigwira ukapolo adatipempha kuti tiimbe nyimbo. Otizunza adatipempha kuti tisangalale, adati, “Tatiimbiraniko nyimbo ya ku Ziyoni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 pakuti anthu otigwira ukapolo anatipempha kuti tiyimbe nyimbo. Otizunza athu anafuna nyimbo zachisangalalo; iwo anati, “Tiyimbireni imodzi mwa nyimbo za ku Ziyoni!” Onani mutuwo |