Masalimo 136:8 - Buku Lopatulika8 Dzuwa liweruze usana; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Dzuwa liweruze usana; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Dzuŵa kuti lizilamulira usana, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Dzuwa lilamulire usana, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |