Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 136:7 - Buku Lopatulika

7 Amene analenga miuni yaikulu; pakuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Amene analenga miuni yaikulu; pakuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Adalenga miyuni yaikulu yamumlengalenga, pakuti chikondi chake nchamuyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Amene anapanga miyuni ikuluikulu, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 136:7
4 Mawu Ofanana  

Anaika mwezi nyengo zake; dzuwa lidziwa polowera pake.


ndi kuti mungakweze maso anu kupenya kumwamba, ndipo poona dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi, khamu lonse la kumwamba, munganyengedwe ndi kuzigwadira, ndi kuzitumikira, zimene Yehova Mulungu wanu anagawira mitundu yonse ya anthu pansi pa thambo lonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa