Masalimo 136:6 - Buku Lopatulika6 Amene anayala dziko lapansi pamwamba pamadzi; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adayala dziko lapansi pa madzi, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |