Masalimo 136:23 - Buku Lopatulika23 Amene anatikumbukira popepuka ife; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Amene anatikumbukira popepuka ife; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Adatikumbukira pamene adani adatigonjetsa, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |