Masalimo 136:24 - Buku Lopatulika24 Natikwatula kwa otisautsa; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Natikwatula kwa otisautsa; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Ndipo adatipulumutsa kwa adani athu, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Amene anatimasula kwa adani athu, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |