Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 136:13 - Buku Lopatulika

13 Amene anagawa magawo Nyanja Yofiira; pakuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Amene anagawa magawo Nyanja Yofiira; pakuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Adagaŵa pakati Nyanja Yofiira, pakuti chikondi chake nchamuyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 136:13
8 Mawu Ofanana  

Mudagawa nyanja ndi mphamvu yanu; mudaswa mitu ya zoopsa za m'madzi.


Anagawa nyanja nawapititsapo; naimitsa madziwo ngati khoma.


Koma ana a Israele anayenda pouma pakati pa nyanja; ndi madziwo anakhala ngati khoma kwa iwo, palamanja ndi lamanzere.


Ndi chikhulupiriro anaoloka Nyanja Yofiira kupita ngati pamtunda: ndiko Aejipito poyesanso anamizidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa