Masalimo 135:6 - Buku Lopatulika6 Chilichonse chimkonda Yehova achichita, kumwamba ndi padziko lapansi, m'nyanja ndi mozama monse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chilichonse chimkonda Yehova achichita, kumwamba ndi pa dziko lapansi, m'nyanja ndi mozama monse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chilichonse chimene Chauta amafuna kuchita amachitadi kumwamba ndi pa dziko lapansi, m'nyanja ndi monse mozama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova amachita chilichonse chimene chimamukomera, kumwamba ndi dziko lapansi, ku nyanja zazikulu ndi ku malo ake onse akuya. Onani mutuwo |