Masalimo 135:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti ndidziwa kuti Yehova ndi wamkulu, ndi Ambuye wathu aposa milungu yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti ndidziwa kuti Yehova ndi wamkulu, ndi Ambuye wathu aposa milungu yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pakuti ndimadziŵa kuti Chauta ndi wamkulu, kuti Chauta, Mulungu wathu, ndi wamphamvu kupambana milungu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndikudziwa kuti Yehova ndi wamkulu, kuti Ambuye athu ndi wamkulu kuposa milungu yonse. Onani mutuwo |