Masalimo 135:3 - Buku Lopatulika3 Lemekezani Yehova; pakuti Yehova ndiye wabwino; muimbire zolemekeza dzina lake; pakuti nkokondweretsa kutero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Lemekezani Yehova; pakuti Yehova ndiye wabwino; muimbire zolemekeza dzina lake; pakuti nkokondweretsa kutero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tamandani Chauta, pakuti ngwabwino. Muimbireni nyimbo zotamanda dzina lake, pakuti nlokoma kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tamandani Yehova, pakuti Yehova ndi wabwino; imbani nyimbo zotamanda dzina lake, pakuti nʼkokoma kutero, Onani mutuwo |