Masalimo 135:19 - Buku Lopatulika19 A nyumba ya Israele inu, lemekezani Yehova: A nyumba ya Aroni inu, lemekezani Yehova: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 A nyumba ya Israele inu, lemekezani Yehova: A nyumba ya Aroni inu, lemekezani Yehova: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Inu a m'banja la Israele, tamandani Chauta! Inu a m'banja la Aroni, tamandani Chauta! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Inu nyumba ya Israeli, tamandani Yehova; inu nyumba ya Aaroni, tamandani Yehova; Onani mutuwo |