Masalimo 135:18 - Buku Lopatulika18 Akuwapanga adzafanana nao; inde, onse akuwakhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Akuwapanga adzafanana nao; inde, onse akuwakhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Anthu amene amapanga mafanowo afanefane nawo, chimodzimodzi onse amene amaŵakhulupirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iwo amene amapanga mafanowo adzakhala ngati mafanowo, chimodzimodzinso iwo amene amadalira mafanowo. Onani mutuwo |