Masalimo 135:17 - Buku Lopatulika17 makutu ali nao, koma osamva; inde, pakamwa pao palibe mpweya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 makutu ali nao, koma osamva; inde, pakamwa pao palibe mpweya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Makutu ali nawo, koma saamva, ndipo alibe mpweya m'kamwa mwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 makutu ali nawo, koma sakumva ndipo mʼkamwa mwawo mulibe mpweya uliwonse. Onani mutuwo |