Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 135:16 - Buku Lopatulika

16 Pakamwa ali napo koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Pakamwa ali napo koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Pakamwa ali napo, koma salankhula, maso ali nawo, koma sapenya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Pakamwa ali napo koma sayankhula maso ali nawo, koma sapenya;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 135:16
2 Mawu Ofanana  

Nenepetsa mtima wa anthu awa, lemeretsa makutu ao, nutseke maso ao; angaone ndi maso ao, angamve ndi makutu ao, angazindikire ndi mtima wao, nakabwerenso, nachiritsidwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa