Masalimo 135:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ake, koma adzaleka atumiki ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ake, koma adzaleka atumiki ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pakuti Chauta adzaweruza anthu ake kuti alibe mlandu, adzachitira chifundo atumiki ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti Yehova adzaonetsa kuti anthu ake ngosalakwa, ndipo adzachitira chifundo atumiki ake. Onani mutuwo |