Masalimo 135:13 - Buku Lopatulika13 Dzina lanu, Yehova, likhala kosatha; chikumbukiro chanu, Yehova, kufikira mibadwomibadwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Dzina lanu, Yehova, likhala kosatha; chikumbukiro chanu, Yehova, kufikira mibadwomibadwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Dzina lanu, Inu Chauta, nlamuyaya, kutchuka kwanu ndi kwa pa mibadwo yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Dzina lanu, Inu Yehova, ndi losatha mpaka muyaya, mbiri yanu, Inu Yehova, idziwika mibado yonse. Onani mutuwo |